Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 8:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ananyamuka napita; ndipo taona munthu wa ku Aitiopiya, mdindo wamphamvu wa Kandake, mfumu yaikazi ya Aaitiopiya, ndiye wakusunga cuma cace conse, amene anadza ku Yerusalemu kudzapemphera;

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 8

Onani Macitidwe 8:27 nkhani