Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 8:15-19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

15. amenewo, m'mene adatsikirako, anawapempherera, kuti alandire Mzimu Woyera:

16. pakuti kufikira pamenepo nkuti asanagwe pa wina mmodzi wa iwo; koma anangobatizidwam'dzina la Ambuye Yesu.

17. Pamenepo anaika manja pa iwo, ndipo analandira Mzimu Woyera.

18. Koma pakuona Simoni kuti mwa kuika manja a atumwi anapatsidwa Mzimu Woyera, anawatengera ndalama,

19. nanena, Ndipatseni inenso ulamuliro umene, kuti amene ali yense ndikaika manja pa iye, alandire Mzimu Woyera.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 8