Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 7:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Mulungu analankhula cotero, kuti mbeu yace idzakhala alendo m'dziko la eni, ndipo adzawacititsa ukapolo, nadzawacitira coipa, zaka mazana anai.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 7

Onani Macitidwe 7:6 nkhani