Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 7:58-60 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

58. ndipo 27 anamtaya kunja kwa mudzi, namponya miyala; ndipo 28 mbonizo zinaika zobvala zao pa mapazi a mnyamata dzina lace Saulo.

59. Ndipo anamponya miyala Stefano, alikuitana Ambuye, ndi kunena, 29 Ambuye Yesu, landirani mzimu wanga.

60. Ndipo m'mene anagwada pansi, anapfuula ndi mau akuru, 30 Ambuye, musawaikire iwo cimo ili. Ndipo m'mene adanena ici, anagona tulo.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 7