Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 4:34-37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

34. Pakuti mwa iwo munalibe wosowa; 1 pakuti onse amene anali nayo minda, kapena nyumba, anazigulitsa nabwera nao malonda ace a izo adazigulitsa,

35. 2 nawaika pa mapazi a atumwi; ndipo anagawira yense monga kusowakwace.

36. Ndipo Yosefe, wochedwa ndi atumwi Bamaba (ndilo losandulika mwana wa cisangalalo), Mlevi, pfuko lace la ku Kupro,

37. pokhala nao munda, anaugulitsa, nabwera nazo ndalama zace, 3 naziika pa mapazi a atumwi.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 4