Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 4:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma pakuona kulimbika mtima kwa Petro ndi Yohane, ndipo pozindikira kuti ndiwo anthu osaphunzira ndi opulukira, anazizwa ndipo anawazindikira, kuti adakhala pamodzi ndi Yesu.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 4

Onani Macitidwe 4:13 nkhani