Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 3:16-18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Ndipo pa cikhulupiriro ca m'dzina lace dzina lacelo linalimbikitsa iye amene mumuona, nimumdziwa; ndipo cikhulupiriro ciri mwa iye cinampatsa kucira konse kumeneku pamaso pa inu nonse.

17. Ndipo tsopano, abale, ndidziwa kuti munacicita mosadziwa, monganso akulu anu.

18. Koma zimene Mulungu analalikiratu m'kamwa mwa aneneri onse, kuti adzamva kuwawa Kristu, iye anakwaniritsa cotero.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 3