Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 28:30-31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

30. Ndipo anakhala zaka ziwiri zamphumphu m'nyumba yace yobwereka, nalandira onse akufika kwa iye,

31. ndi kulalikira Ufumu wa Mulungu, ndi kuphunzitsa za Ambuye Yesu Kristu ndi kulimbika konse, wosamletsa munthu.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 28