Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 27:41 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma pofika pamalo pokomana mafunde awiri, anatsamitsapo ngalawa; ndipo kulikuru kunatsama, ndi kukhala kosasunthika, koma kumakaliro kunasweka ndi mphamvu ya mafunde.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 27

Onani Macitidwe 27:41 nkhani