Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 24:3-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. tizilandira ndi ciyamiko conse, monsemo ndi ponsepo, Felike womveka inu.

4. Koma kuti ndingaonjeze kukulemetsani ndikupempha, ni mutimvere mwacidule ndi cifatso canu.

5. Pakuti tapeza munthuyu ali ngati mliri, ndi woutsa mapanduko kwa Ayuda onse m'dziko lonse lokhalamo anthu, ndi mtsogoleri wa mpanduko wa Anazarene;

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 24