Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 23:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene padauka cipolowe cacikuru, kapitao wamkuru anaopa kuti angamkadzule Paulo, ndipo analamulira asilikari atsike, namkwatule pakati pao, nadze naye kulowa naye m'linga,

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 23

Onani Macitidwe 23:10 nkhani