Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 21:17-19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

17. Ndipo pofika ife ku Yerusalemu, abale anatilandira mokondwera.

18. Ndipo m'mawa mwace Paulo analowa nafe kwa Yakobo; ndi akulu onse anali pomwepo.

19. Ndipo atawalankhula iwo, anawafotokozera cimodzi cimodzi zimene Mulungu anacita kwa amitundu mwa utumiki wace.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 21