14. Ndipo pokana iye kukopeka, tinaleka, ndi kuti, Kufuna kwa Ambuye kucitidwe.
15. Ndipo atapita masiku awa tinakonza akatundu athu, ntikwera ku Yerusalemu.
16. Ndipo anamuka nafenso ena a ophunzira a ku Kaisareya, natenganso wina Mnaso wa ku Kupro, wophunzira wakale, amene adzaticereza.
17. Ndipo pofika ife ku Yerusalemu, abale anatilandira mokondwera.