35. M'zinthu zonse ndinakupatsani citsanzo, cakuti pogwiritsa nchito, koteromuyenerakuthandiza ofoka ndi kukumbuka mau a Ambuye Yesu, kuti anati yekha, Kupatsa kutidalitsa koposa kulandira.
36. Ndipo m'mene ananena izi, anagwada pansi, napemphera ndi iwo onse.
37. Ndipo onsewa analira kwambiri, namkupatira Paulo pakhosi pace, nampsompsona,