Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 20:17-20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

17. Ndipo pokhala ku Mileto anatuma ku Efeso, naitana akulu a Mpingo.

18. Ndipo pamene anafika kuli iye, anati kwa iwo,Mudziwa inu kuyambira tsiku loyamba ndinafika ku Asiya, makhalidwe anga pamodzi ndi inu nthawi yonse,

19. wotumikira Ambuye ndi kudzicepetsa konse ndi misozi, ndi mayesero anandigwera ndi ziwembu za Ayuda;

20. kuti sindinakubisirani zinthu zopindulira, osazilalikira kwa inu, ndi kukuphunzitsani inu pabwalo ndi m'nyumba m'nyumba,

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 20