Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 17:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma iwo amene anaperekeza Paulo anadza naye kufikira ku Atene; ndipo polandira iwo lamulo la kwa Sila ndi Timoteo kuti afulumire kudza kwa iye ndi cangu conse, anacoka.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 17

Onani Macitidwe 17:15 nkhani