Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 17:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma pamene Ayuda a ku Tesalonika anazindikira kuti mau a Mulungu analalikidwa ndi Paulo ku Bereyanso, anadza komwekonso, nautsa, nabvuta makamu.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 17

Onani Macitidwe 17:13 nkhani