Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 16:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anacita cotero masiku ambiri. Koma Paulo anabvutika mtima ndithu, naceuka, nati kwa mzimuwo, Ndikulamulira iwe m'dzina la Yesu Kristu, turuka mwa iye. Ndipo unaturuka nthawi yomweyo.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 16

Onani Macitidwe 16:18 nkhani