Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 15:37-41 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

37. Ndipo Bamaba anafuna kumtenga Yohane uja, wochedwa Marko.

38. Koma sikunamkomera Paulo kumtenga iye amene anawasiya nabwerera pa Pamfuliya paja osamuka nao kunchito.

39. Ndipo panali kupsetsana mtima, kotero kuti analekana wina ndi mnzace; ndipo Bamaba anatenga Marko, nalowa n'ngalawa, nanka ku Kupro.

40. Koma Paulo anasankha Sila, namuka, woikizidwa ndi abale ku cisomo ca Ambuye.

41. Ndipo iye anapita kupyola pa Suriya ndi Kilikiya, nakhazikitsa Mipingo.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 15