Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 14:6-11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. iwo anamva, nathawira ku midzi ya Lukaoniya, Lustra ndi Derbe, ndi dziko lozungulirapo:

7. kumeneko ndiko Uthenga Wabwino.

8. Ndipo pa Lustra panakhala munthu wina wopanda mphamvu ya m'mapazi mwace, wopunduka cibadwire, amene sanayenda nthawi zonse.

9. Ameneyo anamva Paulo alinkulankhula; ndipo Paulo pomyang'anitsa, ndi kuona kuti anali ndi cikhulupiriro colandira naco moyo,

10. anati ndi mau akuru, Taimirira. Ndipo iyeyu anazunzuka, nayenda.

11. Pamene makamu anaona cimene anacita Paulo, anakweza mau ao, nati m'cinenero ca Lukaoniya, Milungu yatsikira kwa ife monga anthu.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 14