Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 14:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace anakhala nthawi yaikuru nanenetsa zolimba mtima mwa Ambuye, amene anacitira umboni mau a cisomo cace, napatsa zizindikiro ndi zozizwa kuti zicitidwe ndi manja ao.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 14

Onani Macitidwe 14:3 nkhani