Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 14:18-20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

18. Pakunena izo, anabvutika pakuletsa makamu kuti asapereke nsembe kwa iwo.

19. Ndipo anafika kumeneko Ayuda kucokera ku Antiokeya ndi Ikoniyo; nakopa makamu, ndipo anamponya Paulomiyala, namguzira kunja kwa mudzi; namuyesa kuti wafa.

20. Koma pamene, anamzinga akuphunzirawo, anauka iye, nalowa m'mudzi; m'mawa mwace anaturuka ndi Bamaba kunka, ku Derbe.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 14