Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 11:28-30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

28. Ndipo anyanamuka mmodzi wa iwo, dzina lace Agabo, nalosa mwa Mzimu, kuti padzakhala njala yaikulu pa dziko lonse lokhalamo anthu; ndiyo idadza masiku a Klaudiyo.

29. Ndipo akuphunzira, yense monga anakhoza, anatsimikiza mtima kutumiza zothandiza abale akukhala m'Yudeya;

30. iconso anacita, natumiza kwa akulu mwa dzanja la Bamaba ndi Saulo.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 11