Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 10:8-11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

8. ndipo m'mene adawafotokozerazonse, anawatuma ku Yopa.

9. Koma m'mawa mwace, pokhala paulendo pao iwowa, m'mene anayandikira mudzi, Petro anakwera pachindwi kukapemphera, ngati pa ora lacisanu ndi cimodzi; ndipo anagwidwa njala, nafuna kudya;

10. koma m'mene analikumkonzera cakudya kudamgwera ngati kukomoka;

11. ndipo anaona pathambo padatseguka, ndi cotengera cirinkutsika, conga ngati cinsaru cacikuru, cogwiridwa pa ngondya zace zinai, ndi kutsikira padziko pansi;

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 10