Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 9:52-55 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

52. natumiza amithenga patsogolo pace; ndipo ananka, nalowa m'mudzi wa Asamariya, kukamkonzera iye malo.

53. Ndipo iwo sanamlandira iye, cifukwa nkhope yace inali yoloza kunka ku Yerusalemu.

54. Ndipo pamene ophunzira ace Yakobo ndi Yohane anaona, anati, Ambuye, Kodi mufuna kuti ife tiuze mota utsike kumwamba ndi kuwanyeketsa iwo?

55. Koma iye anapotoloka nawadzudzula.

Werengani mutu wathunthu Luka 9