Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 9:42 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo akadadza iye, ciwandaco cinamgwetsa, ndi kumng'ambitsa, Koma Yesu anadzudzula mzimu wonyansawo, naciritsa mnyamata, nambwezera iye kwa atate wace.

Werengani mutu wathunthu Luka 9

Onani Luka 9:42 nkhani