Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 9:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

nati, Kuyenera kuti Mwana wa munthu amve zowawa zambiri, ndi kukanidwa ndi akuru, ndi ansembe akuru, ndi alembi, ndi kuphedwa, ndi kuuka tsiku lacitatu.

Werengani mutu wathunthu Luka 9

Onani Luka 9:22 nkhani