Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 8:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo zina zinagwa pa nthaka yokoma, ndipo zinamera, ndi kupatsa zipatso zamakumikhumi. Pakunena iye izi anapfuula, iye amene ali ndi makutu akumva amve.

Werengani mutu wathunthu Luka 8

Onani Luka 8:8 nkhani