53. Ndipo anamseka iye pwepwete podziwa kuti anafa.
54. Ndipo iye anamgwira dzanja lace, naitana, nati, Buthu, tauka.
55. Ndipo mzimu wace unabwera, ndipo anauka pomwepo; ndipo iye anawauza kuti ampatse kanthu ka kudya.
56. Ndipo atate wace ndi amace anadabwa; ndipo analamulira iwo asauze munthu ali yense cimene cinacitika.