Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 8:52-54 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

52. Ndipo anthu onse analikumlira iye ndi kudzigugudapacifuwa. Koma iye anati, Musalire; pakuti iye sanafa, koma agona tulo.

53. Ndipo anamseka iye pwepwete podziwa kuti anafa.

54. Ndipo iye anamgwira dzanja lace, naitana, nati, Buthu, tauka.

Werengani mutu wathunthu Luka 8