Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 8:47 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mkaziyo pakuona kuti sanabisika, anadza ndi kunthunthumira, nagwa pamaso pace, nafotokoza pamaso pa anthu onsewo cifukwa cace ca kumkhudza iye, ndi kuti anaciritsidwa pomwepo.

Werengani mutu wathunthu Luka 8

Onani Luka 8:47 nkhani