Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 8:45 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yesu anati, Wandikhudza Ine ndani? Koma pamene onse anakana, Petro ndi iwo akukhala naye anati, Ambuye, anthu aunyinji alikukankhana pa Inu ndi kukanikizana.

Werengani mutu wathunthu Luka 8

Onani Luka 8:45 nkhani