Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 8:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iye anati kwa iwo, Cikhulupiriro canu ciri kuti? Ndipo m'kucita mantha anazizwa iwo, nanena wina ndi mnzace, Uyu ndani nanga, kuti angolamula mphepo ndi madzi, ndipo zimvera iye?

Werengani mutu wathunthu Luka 8

Onani Luka 8:25 nkhani