Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 8:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panali limodzi la masiku aja, iye analowa m'ngalawa, ndi ophunzira ace; nati kwa iwo, Tiolokere ku tsidya lija la nyanja; ndipo anakankhiramo.

Werengani mutu wathunthu Luka 8

Onani Luka 8:22 nkhani