Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 7:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Yesu pakumva zimenezo anazizwa naye, napotolokera kwa anthu a mpingo wakumtsata iye, nati, Ndinena kwa inu, sindinapeza, ngakhale mwa Israyeli, cikhulupiriro cacikuru cotere.

Werengani mutu wathunthu Luka 7

Onani Luka 7:9 nkhani