Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 7:1-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Pamene Yesu adamariza mau ace onse m'makutu a anthu, analowa m'Kapernao.

2. Ndipo kapolo wa kenturiyo, wokondedwa naye, anadwala, nafuna kutsirizika.

3. Ndipo pamene iye ana-I mva za Yesu, anatuma kwa iye akuru a Ayuda, namfunsa iye kuti adze kupulumutsa kapolo wace.

4. Ndipo iwo, pakufika kwa Yesu, anampempha iye koumirira, nati, Ayenera iye kuti mumcitire ici;

5. pakuti akonda mtundu wathu, ndipo anatimangira ife sunagoge.

Werengani mutu wathunthu Luka 7