Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 6:38 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6 Patsani, ndipo kudzapatsidwa kwa inu; muyeso wabwino, wotsendereka, wokucumuka, wosefukira, anthu adzakupatsani m'manja mwanu. Pakuti 7 kudzayesedwa kwa inu ndi muyeso womwewo muyesa nao inu.

Werengani mutu wathunthu Luka 6

Onani Luka 6:38 nkhani