Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 5:33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iwo anati kwa iye, Ophunzira a Yohane amasala kudya kawiri kawiri, ndi kucita mapemphero; cimodzimodzinso iwo a Afarisi; koma anu amangokudya ndi kumwa.

Werengani mutu wathunthu Luka 5

Onani Luka 5:33 nkhani