Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 5:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panali tsiku limodzi la masiku awo, iye analikuphunzitsa; ndipo analikukhalapo Afarisi ndi aphunzitsi a malamulo, amene anacokera ku midzi yonse ya ku Galileya, ndi Yudeya ndi Yerusalemu: ndipo mphamvu ya Ambuye inali ndi iye yakuwaciritsa,

Werengani mutu wathunthu Luka 5

Onani Luka 5:17 nkhani