Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 24:50-53 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

50. Ndipo anaturuka nao kufikira ku Betaniya; nakweza manja ace, nawadalitsa.

51. Ndipo kunali, 13 pakuwadalitsa iye analekana nao, natengedwa kunka Kumwamba.

52. Ndipo 14 anamlambira iye, nabwera ku Yerusalemu ndi cimwemwe cacikuru;

53. ndipo IS anakhala ci khalire m'Kacisi, nalikuyamika Mulungu, Amen.

Werengani mutu wathunthu Luka 24