Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 21:36-38 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

36. Koma inu dikirani nyengo zonse ndi kupemphera, kutimukalimbike kupulumuka zonse zimene zidzacitika, ndi kuimirira pamaso pa Mwana wa munthu.

37. Ndipo usana uli wonse iye analikuphunzitsa m'Kacisi; ndi usiku uli wonse anaturuka, nagona pa phiri lochedwa la Azitona.

38. Ndipo anthu onse analawira mamawa kudza kwa iye kuKacisi kudzamvera Iye.

Werengani mutu wathunthu Luka 21