Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 21:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma zisanacitike izi, anthu adzakuthirani manja, nadzakuzunzani, nadzapereka inu ku masunagoge ndi ndende, nadzamuka nanu kwa mafumu ndi akazembe, cifukwa ca dzina langa.

Werengani mutu wathunthu Luka 21

Onani Luka 21:12 nkhani