Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 20:40-43 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

40. Pakuti sanalimbanso mtima kumfunsa iye kanthu kena.

41. Koma iye anati kwa iwo, Amanena bwanji kuti Kristuyo ndiye mwana wa Davine?

42. Pakuti Davine yekha anena m'buku la Masalmo,Ambuye ananena kwa Ambuye wanga,Ukhale pa dzanja langa lamanja,

43. Kufikira Ine ndikaika adani akopansi pa mapazi ako.

Werengani mutu wathunthu Luka 20