Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 19:40-43 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

40. Ndipo anayankha nati, Ndinena ndi inu, ngati awa akhala cete miyala idzapfuula.

41. Ndipo m'meneanayandikira, anaona mudziwo naulirira,

42. nanena, Ukadazindikira tsiku ili, inde iwetu zinthu za mtendere! koma tsopano zibisika pamaso pako.

43. Pakuti masiku adzakudzera, ndipo adani ako adzakuzingira linga, nadzakuzungulira iwe kwete, nadzakutsekereza ponsepo;

Werengani mutu wathunthu Luka 19