Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 19:32-36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

32. Ndipo anacoka otumidwawo, napeza monga adanena kwa iwo.

33. Ndipo pamene anamasula mwana wa buru, eni ace anati kwa iwo, Mumasuliranji mwana wa buru?

34. Ndipo anati, Ambuye amfuna iye.

35. Ndipo anadzanave kwa Yesu; ndipo anayalika zobvala zao pa mwana wa buruyo, nakwezapo Yesu.

36. Ndipo pakupita iye, anayala zobvala zao m'njira.

Werengani mutu wathunthu Luka 19