Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 19:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pakumva izi iwo, iye anaonjeza nanena fanizo, cifukwa anali iye pafupi pa Yerusalemu, ndipo iwo anayesa kuti Ufumu wa Mulungu ukuti uonekere pomwepo.

Werengani mutu wathunthu Luka 19

Onani Luka 19:11 nkhani