Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 18:38-43 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

38. Ndipo anapfuula, nanena, Yesu, Mwana wa Davine, mundicitire cifundo.

39. Ndipo iwo akutsogolera anamdzudzula iye, kuti akhale cete; koma iye anapfuulitsa cipfuulire, Mwana wa Davine, mundicitire cifundo.

40. Ndipo Yesu anaima, nalamulira kuti abwere naye kwa iye: ndipo m'mene adafika pafupi, anamfunsa iye,

41. Of una ndikucitire ciani? Ndipo anati, Ambuye, kuti ndipenyenso.

42. Ndipo Yesu anati kwa iye, Penyanso: cikhulupiriro cako cakupulumutsa iwe.

43. Ndipo pomwepo anapenyanso, namtsata iye, ndi kulemekeza Mulungu: ndipo anthu onse pakuona, anacitira Mulungu mayamiko.

Werengani mutu wathunthu Luka 18