Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 18:31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anadzitengera khumi ndi awiriwo, nati kwa iwo, Taonani, tikwera kunkaku Yerusalemu, ndipo zidzakwaniritsidwa kwa Mwana wa munthu zonse zolembedwa ndi aneneri.

Werengani mutu wathunthu Luka 18

Onani Luka 18:31 nkhani