Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 17:9-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. Kodi ayamika kapoloyocifukwa anacita zolamulidwa?

10. Cotero Inunso m'mene mutacita zonse anakulamulirani, Denani, Ife ndife akapolo opanda pace, tangocita zimene tayenera kuzicita.

11. Ndipo kunali, pakumuka ku Yerusalemu iye analikupita pakati pa Samariya ndi Galileya.

12. Ndipo m'mene analowa iye m'mudzi wina, anakomana naye amuna khumi akhate, amene anaima kutali;

13. ndipo iwo anakweza mau, nanena, Yesu, Mbuye, muticitire cifundo.

Werengani mutu wathunthu Luka 17