Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 17:34-37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

34. Ndinena ndi inu, usiku womwewo adzakhala awiri pa kama mmodzi; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa.

35. Padzakhala akazi awiri akupera pamodzi, mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa. [

36. ]

37. Ndipo anayankha nanena kwa iye, Kuti, Ambuye? Ndipo anati kwa iwo, Pamene pali mtembo, pomweponso miimba idzasonkhanidwa.

Werengani mutu wathunthu Luka 17